Jeremiah 2:32 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi namwali amaiŵala zokongoletsera zake, kapena mkwati kuiŵala zovala zake zaukwati? Komabe anthu anga andiiŵala Ine masiku osaŵerengeka.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kodi angathe namwali kuiwala zokometsera zake, kapena mkwitibwi zovala zake? Koma anthu anga andiiwala Ine masiku osawerengeka.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi namwali amayiwala zokongoletsera zake, kapena kuyiwala zovala zake za ukwati? Komatu anthu anga andiyiwala masiku osawerengeka.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kodi angathe namwali kuiwala zokometsera zace, kapena mkwatibwi zobvala zace? koma anthu anga andiiwala Ine masiku osawerengeka.