Jeremiah 20:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Wansembe Pasuri, mwana wa Imeri, amene anali kapitao wamkulu ku Nyumba ya Chauta, adamva Yeremiya akulosa zinthu zimenezi.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Pasuri mwana wake wa Imeri wansembe, amene anali kapitao wamkulu m'nyumba ya Yehova, anamva Yeremiya alikunenera zimenezi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wansembe Pasuri mwana wa Imeri, woyangʼanira wamkulu wa Nyumba ya Yehova, anamva Yeremiya akulosera zinthu zimenezi.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Pasuri mwana wace wa Imeri wansembe, amene anali kapitao wamkuru m'nyumba ya Yehova, anamva Yeremiya alikunenera zimenezi.