Jeremiah 20:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsoka kwa iye amene adakasangalatsa bambo wanga ndi uthenga woti, “Kunyumba kwanu kwabadwa mwana wamwamuna.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Atembereredwe munthu amene anatengera mau kwa atate wanga, kuti, Mwana wamwamuna anakubadwira iwe; ndi kumsekeretsatu iye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Wotembereredwa munthu amene anapita kukasangalatsa abambo anga ndi uthenga woti: “Kwabadwa mwana wamwamuna!”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Atembereredwe munthu amene anatengera mau kwa atate wanga, kuti, Mwana wamwamuna anakubadwira iwe; ndi kumsekeretsatu iye.