Jeremiah 21:3 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma otumidwa aja atafika, Yeremiya adaŵauza kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yeremiya anati kwa iwo, Muzitero kwa Zedekiya:
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Yehova anawuza Yeremiya kuti ayankhe Pasuri ndi Zefaniya kuti, “Kamuwuzeni Zedekiya kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yeremiya anati kwa iwo, Muzitero kwa Zedekiya: