Jeremiah 22:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adandiwuza kuti, “Pita ku nyumba ya mfumu ya ku Yuda, ukaiwuze kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Yehova atero: Tsikira kunyumba ya mfumu ya Yuda, ndi kunena komweko mau awa,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anandiwuza kuti, “Pita ku nyumba ya mfumu ya ku Yuda ndipo ukayiwuze kuti,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Yehova atero: Tsikira ku nyumba ya mfumu ya Yuda, ndi kunena komweko mau awa,