Jeremiah 22:16 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ankateteza anthu otsika ndi osauka, ndipo zonse zinkamuyendera bwino. Kodi zimenezi sizidaonetse kuti ankandidziŵa?” Akuterotu Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iye anaweruza mlandu wa aumphawi ndi osowa; kumeneko kunali kwabwino. Kodi kumeneko si kundidziwa Ine? Ati Ambuye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iye ankateteza anthu osauka ndi osowa, ndipo zonse zinkamuyendera bwino. Kodi zimenezi sindiye tanthauzo la kudziwa Ine?” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iye anaweruza mlandu wa aumphawi ndi osowa; kumeneko kunali kwabwino. Kodi kumeneko si kundidziwa Ine? ati Ambuye.