Jeremiah 22:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Adzamuika ngati bulu basi, kuchita kumguguza nkukamtaya kuseri kwa zipata za Yerusalemu.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Adzamuika monga kuika bulu, adzamkoka nadzamponya kunja kwa zipata za Yerusalemu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Adzayikidwa ngati bulu, kuchita kumuguguza ndi kukamutaya kunja kwa zipata za Yerusalemu.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Adzamuika monga kuika buru, adzamkoka nadzamponya kunja kwa zipata za Yerusalemu.