Jeremiah 22:23 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Inu amene mumakhala ku nyumba ya ku Lebanoni ija, amene mudamanga nyumba zanu pakati pa mikungudza, mudzalira kwambiri pamene zoŵaŵa zidzakugwerani, zonga za mkazi pa nthaŵi yake yochira.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Iwe wokhala m'Lebanoni, womanga chisa chako m'mikungudza, udzachitidwa chisoni chachikulu nanga pamene mapweteko adzadza kwa iwe, monga mkazi alinkudwala!
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Inu amene mumakhala mʼnyumba ya ku Lebanoni, amene munamanga nyumba zanu pakati pa mikungudza, mudzabuwula kwambiri pamene zowawa zidzakugwerani, zonga za mkazi pa nthawi yake yochira!
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Iwe wokhala m'Lebano, womanga cisa cako m'mikungudza, udzacitidwa cisoni cacikuru nanga pamene mapweteko adzadza kwa iwe, monga mkazi alinkudwala!