Jeremiah 22:8 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Pamene anthu a mitundu ina adzadutse pa mzinda umenewu, azidzafunsana kuti, ‘Kodi chifukwa chiyani Chauta adaononga chotere mzinda waukuluwu?’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo amitundu ambiri adzapita pa mudzi uwu, nadzati yense kwa mnzake, Yehova anatero nao mudzi waukulu uwu chifukwa ninji?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Pamene anthu a mitundu ina adzadutsa pa mzinda umenewu adzafunsana kuti, ‘Chifukwa chiyani Yehova wachita chinthu chotere pa mzinda waukuluwu?’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo amitundu ambiri adzapita pa mudzi uwu, nadzati yense kwa mnzace, Yehova anatero nao mudzi waukuru uwu cifukwa ninji?