Jeremiah 23:22 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akadakhala nane pa bungwe langa, bwenzi atalalikadi mau anga kwa anthu anga. Bwenzi ataŵachotsa m'njira zao zoipa, kuti aleke machimo ao.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma akadaima m'upo wanga, akadamvetsa anthu anga mau anga, akadatembenuza iwo kunjira yao yoipa, ndi kuchoipa cha ntchito zao.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Iwo akanakhala pa msonkhano wanga ndiye kuti akanamayankhula mawu anga kwa anthu anga. Komanso bwenzi atawachotsa anthu anga mʼnjira zawo zoyipa kuti aleke machimo awo.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma akadaima m'upo wanga, akadamvetsa anthu anga mau anga, akadatembenuza iwo ku njira yao yoipa, ndi ku coipa ca nchito zao.