Jeremiah 23:30 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Nchifukwa chake ndikuŵakana aneneri amene amaberana mau iwo okhaokha nkumati mauwo ndi a Ineyo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Chifukwa chake, taonani, Ine ndidana ndi aneneri, ati Yehova, amene amaba mau anga, yense kumbera mnansi wake.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova akuti, “Nʼchifukwa chake, Ine ndikudana nawo aneneri amene amaberana okhaokha mawu nʼkumati mawuwo ndi a Yehova.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Cifukwa cace, taonani, Ine ndidana ndi aneneri, ati Yehova, amene amaba mau anga, yense kumbera mnansi wace.