Jeremiah 25:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Kenaka udzaŵauze kuti, Chauta Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israele, akunena kuti, ‘Imwani, muledzere, musanze, mugwe osadzukanso, chifukwa cha nkhondo imene ndikutumiza pakati panu.’ ”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo uziti kwa iwo, Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele: Imwani inu, ndi kuledzera, ndi kusanza, ndi kugwa, osanyamukanso konse, chifukwa cha lupanga limene ndidzatumiza mwa inu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ndipo uwawuze kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli akuti: Imwani, ledzerani ndipo musanze, mugwe osadzukanso chifukwa cha nkhondo imene ndikutumiza pakati panu.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo uziti kwa iwo, Atero Yehova wa makamu, Mulungu wa Israyeli: Imwani inu, ndi kuledzera, ndi kusanza, ndi kugwa, osanyamukanso konse, cifukwa ca lupanga limene ndidzatumiza mwa inu.