Jeremiah 25:28 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Akakana kulandira chikho kumanja kwako kuti amwe, uŵauze kuti, Chauta Wamphamvuzonse akunena kuti, Muyenera kumwa!
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo padzakhala, ngati akana kutenga chikho pa dzanja lako kuti amwe, uziti kwa iwo, Yehova wa makamu atero: Kumwa muzimwa,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma ngati akana kutenga chikhocho mʼdzanja lako ndi kumwa, uwawuze kuti, ‘Yehova Wamphamvuzonse akuti: Muyenera kumwa ndithu!’ ”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo padzakhala, ngati akana kutenga cikho pa dzanja lako kuti amwe, uziti kwa iwo, Yehova wa makamu atero: Kumwa muzimwa.