Jeremiah 26:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Yeremiya adauza akuluakulu aja ndi anthu onse kuti, “Chauta adachita kundituma kuti ndilengeze mau onse mwamvaŵa oinena Nyumba ya Mulungu ino pamodzi ndi mzindawu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo Yeremiya ananena kwa akulu onse ndi kwa anthu onse, kuti, Yehova anandituma ine ndinenere nyumba iyi ndi mudzi uwu mau onse amene mwamva.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndipo Yeremiya anawuza nduna zija ndi anthu onse kuti, “Yehova anandituma kunenera mawu onse amene mwawamva otsutsa Nyumba ino ndi mzinda uno.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo Yeremiya ananena kwa akuru onse ndi kwa anthu onse, kuti, Yehova anandituma ine ndinenere nyumba iyi ndi mudzi uwu mau onse amene mwamva.