Jeremiah 26:5 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
ngati simumvera mau a aneneri, atumiki anga, amene ndakhala ndikuŵatuma kwa inu, ngakhale kuti inu simunkaŵamvera,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
kumvera mau a atumiki anga aneneri, amene ndituma kwa inu, pouka mamawa ndi kuwatuma iwo, koma simunamvera;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo ngati simumvera mawu a atumiki anga, aneneri amene ndakhala ndikukutumizirani, ngakhale kuti simunawamvere,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
kumvera mau a atumiki anga aneneri, amene ndituma kwa inu, pouka mamawa ndi kuwatuma iwo, koma simunamvera;