Jeremiah 27:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta Wamphamvuzonse ndiye akunena za mizati, chimbiya, maphaka ndi ziŵiya zonse zimene zidatsala mumzindamu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Yehova wa makamu atero, za zoimiritsa, ndi za thawale, ndi za zoikirapo, ndi za zipangizo zotsala m'mudzi uwu,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Pakuti Yehova akunena za zipilala, za mbiya ya madzi, maphaka ndi ziwiya zina zimene zatsala mu Yerusalemu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yehova wa makamu atero, za zoimiritsa, ndi za thawale, ndi za zoikirapo, ndi za zipangizo zotsala m'mudzi uwu,