Jeremiah 30:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Palibe amene angathe kukutetezani pa mlandu wanu. Palibe mankhwala opoletsa chilonda chanu. Palibe mankhwala ochiza nthenda yanu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Palibe amene adzanenera mlandu wako, ulibe mankhwala akumanga nao bala lako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Palibe amene angathe kukutetezani pa mlandu wanu, palibe chiyembekezo choti inu nʼkuchira, palibe mankhwala ochiritsa inu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Palibe amene adzanenera mlandu wako, ulibe mankhwala akumanga nao bala lako.