Jeremiah 30:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Tamva kulira kwankhaŵa, kufuula kwamantha, ndipo palibe mtendere paliponse.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Yehova atero: Tamva ife mau akunthunthumira, ndi amantha, si amtendere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Yehova akuti: “Ndamva kulira chifukwa cha nkhawa, ndamva kulira kwa mantha popeza palibe mtendere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yehova atero: Tamva ife mau akunthunthumira, ndi amantha, si amtendere.