Jeremiah 30:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Funsani kuti muzindikire, Kodi munthu wamwamuna angathe kubala mwana? Nanga nchifukwa chiyani ndikuwona munthu wamwamuna aliyense atagwira manja pa mimba ngati mkazi pa nthaŵi yake yochira? Chifukwa chiyani nkhope zonse zagwa?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Funsani tsopano, ndi kuona ngati mwamuna aona mwana; chifukwa chanji ndiona mwamuna ndi manja ake pa chuuno chake, monga mkazi alinkubala, ndi nkhope zao zotumbuluka?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono khalani pansi ndi kudzifunsa kuti: Kodi munthu wamwamuna angathe kubereka mwana? Nanga nʼchifukwa chiyani ndikuona munthu aliyense wamwamuna atagwira manja ake pa mimba pake ngati mayi pa nthawi yake yochira? Chifukwa chiyani nkhope iliyonse ili yakugwa?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Funsani tsopano, ndi kuona ngati mwamuna aona mwana; cifukwa canji ndiona mwamuna ndi manja ace pa cuuno cace, monga mkazi alinkubala, ndi nkhope zao zotumbuluka?