Jeremiah 31:38 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akuti, “Ikubwera nthaŵi pamene mzinda uja wa Chauta udzamangidwanso kuyambira ku Nsanja ya Hananele mpaka ku Chipata cha Ngodya.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taonani, masiku adza, ati Yehova, amene mudziwu udzamangidwira Yehova kuyambira pa nsanja ya Hananele kufikira kuchipata cha kungodya.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Taonani masiku akubwera,” akutero Yehova, “pamene mzinda wa Yehova udzamangidwanso kuyambira ku Nsanja ya Hananeli mpaka ku Chipata cha Ngodya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taonani, masiku adza, ati Yehova, amene mudziwu udzamangidwira Yehova kuyambira pa nsanja ya Hananeli kufikira ku cipata ca kungondya.