Jeremiah 32:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ine ndine Chauta, Mulungu wa anthu onse. Kodi chilipo choti Ine nkundikanika?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Taona, Ine ndine Yehova, Mulungu wa anthu onse; kodi kuli kanthu kondilaka Ine?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Taonani, Ine ndine Yehova, Mulungu wa anthu onse. Kodi chilipo chinthu choti Ine nʼkundikanika?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Taona, Ine ndine Yehova, Mulungu wa anthu lonse; kodi kuli kanthu kondilaka Ine?