Jeremiah 32:40 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzachita nawo chipangano chosatha. Sindidzaleka kuŵachitira zabwino. Ndidzaŵapatsa mtima wondiwopa, motero sadzandisiyanso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndipo ndidzapangana nao pangano lamuyaya, kuti sindidzawachokera kuleka kuwachitira zabwino; koma ndidzalonga kuopsa kwanga m'mitima yao, kuti asandichokere.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndidzachita nawo pangano losatha: sindidzaleka kuwachitira zabwino, ndipo ndidzawapatsa mtima woti azidzandiopa, kuti asadzandisiyenso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndipo ndidzapangana nao pangano lamuyaya, kuti sindidzawacokera kuleka kuwacitira zabwino; koma ndidzalonga kuopsa kwanga m'mitima yao, kuti asandicokere.