Jeremiah 35:16 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ana a Yonadabu, mwana wa Rekabu, adatsata lamulo limene kholo lao lidaŵapatsa. Koma inuyo simudandimvere ai.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti monga ana a Yonadabu mwana wa Rekabu achita lamulo la kholo lao limene anawauza, koma anthu awa sanandimvere Ine.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Zidzukulu za Yehonadabu mwana wa Rekabu zakhala zikumvera lamulo limene kholo lawo anazilamula, koma inuyo simunandimvere Ine.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti monga ana a Yonadabu mwana wa Rekabu acita lamulo la kholo lao limene anawauza, koma anthu awa sanandimvera Ine.