Jeremiah 35:7 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Musadzamange nyumba kapena kubzala mbeu, kapena kulima minda yamphesa. Zinthu zimenezi musadzakhale nazo. M'malo mwake muzidzangokhala m'mahema pa moyo wanu wonse, kuti mukhale nthaŵi yaikulu m'dziko limene mukukhalamo.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndiponso musamange nyumba, musafese mbeu, musaoke mipesa, musakhale nayo; koma masiku anu onse mudzakhale m'mahema; kuti mukhale ndi moyo masiku ambiri m'dziko limene mukhalamo alendo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Musadzamange nyumba kapena kufesa mbewu, kapena kulima minda ya mpesa; musadzakhale ndi zinthu zimenezi. Mʼmalo mwake muzidzakhale mʼmatenti. Mukadzatero mudzakhala nthawi yayitali mʼdziko limene mukukhalamo.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndiponso musamange nyumba, musafese mbeu, musaoke mipesa, musakhale nayo; koma masiku anu onse mudzakhale m'mahema; kuti mukhale ndi moyo masiku ambiri m'dziko limene mukhalamo alendo.