Jeremiah 36:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma tatiwuza, m'mene udalembera mau onseŵa. Kodi ndi Yeremiya adakulembetsa zimenezitu ati?”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anamfunsa Baruki, kuti, Utifotokozeretu, Unalemba bwanji mau awa onse ponena iye?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono anamufunsa Baruki kuti, “Tatiwuze, unalemba bwanji mawu onsewa? Kodi ndi Yeremiya anakulembetsa zimenezi?”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anamfunsa Baruki, kuti, Utifotokozeretu, Unalemba bwanji mau awa onse ponena iye?