Jeremiah 36:4 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Yeremiya adaitana Baruki mwana wa Neriya. Ndipo Barukiyo adalemba m'bukumo mau onse amene Yeremiya ankamuuza, ndiye kuti mau onse amene Chauta adalankhula ndi Yeremiyayo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yeremiya anaitana Baruki mwana wa Neriya; ndipo Yeremiya analembetsa Baruki m'buku lampukutu mau onse a Yehova, amene ananena naye.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Yeremiya anayitana Baruki mwana wa Neriya. Baruki analemba mʼbuku mawu onse amene Yeremiya ankamuwuza, mawu amene Yehova anamuwuza Yeremiya.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yeremiya anaitana Baruki mwana wa Neriya; ndipo Yeremiya analembetsa Baruki m'buku lampukutu mau onse a Yehova, amene ananena naye.