Jeremiah 4:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ngati mukufuna kubwerera, inu Aisraele, bwererani kwa Ine,” akuterotu Chauta. “Chotsani mafano anu amene akundinyansaŵa, ndipo musasokerenso.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ngati udzabwera, Israele, ati Yehova, udzabwera kwa Ine; ndipo ngati udzachotsa zonyansa zako pamaso panga sudzachotsedwa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Ngati mukufuna kubwerera, inu Aisraeli, bwererani kwa Ine,” akutero Yehova. “Chotsani mafano anu onyansa pamaso panga ndipo musasocherenso.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ngati udzabwera, Israyeli, ati Yehova, udzabwera kwa Ine; ndipo ngati udzacotsa zonyansa zako pamaso panga sudzacotsedwa.