Jeremiah 4:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Akuzinga Yerusalemu ngati alonda a munda, chifukwa choti anthu andipandukira,” akuterotu Chauta.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Monga adindo a m'munda amzinga iye; chifukwa andipandukira Ine, ati Yehova.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Azinga Yerusalemu ngati anthu olondera munda, chifukwa Yerusalemu wandiwukira,’ ” akutero Yehova.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Monga adindo a m'munda amzinga iye; cifukwa andipandukira Ine, ati Yehova.