Jeremiah 4:21 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Kodi ndikhale ndikuwona mbendera yankhondo mpaka liti? Kodi ndikhale ndikumva lipenga mpaka liti?
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kufikira liti ndidzaona mbendera, ndi kumva kulira kwa lipenga?
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kodi ndikhale ndikuona mbendera ya nkhondo, ndi kumva kulira kwa lipenga mpaka liti?
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kufikira liti ndidzaona mbendera, ndi kumva kulira kwa lipenga?