Jeremiah 4:25 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidayang'ana, osaona ndi munthu mmodzi yemwe, ndipo mbalame zonse zamumlengalenga zinali zitathaŵa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndinaona, ndipo taona, panalibe munthu, ndi mbalame zonse zakumwamba zinathawa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndinayangʼana, ndipo sindinaone anthu; mbalame iliyonse ya mlengalenga inali itathawa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndinaona, ndipo taona, panalibe munthu, ndi mbalame zonse zakumwamba zinathawa.