Jeremiah 4:27 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta akunena kuti, “Dziko lonse lidzasanduka chipululu, komabe sindidzaliwononga kotheratu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pakuti Yehova atero, Dziko lonse lidzakhala bwinja koma sindidzatsirizitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova akuti, “Dziko lonse lidzasanduka chipululu komabe sindidzaliwononga kotheratu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pakuti Yehova atero, Dziko lonse lidzakhala bwinja koma sindidzatsirizitsa.