Jeremiah 4:5 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Lalika ku Yuda, lengeza ku Yerusalemu kuti, “Lizani lipenga m'dziko lonse, ndi kufuula kuti, ‘Sonkhanani, tiyeni tipite ku mizinda ku Ziyoni.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Nenani m'Yuda, lalikirani m'Yerusalemu, ndi kuti, Ombani lipenga m'dzikomo; fuulani, ndi kuti, Sonkhanani pamodzi, tilowe m'midzi ya malinga.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Lengeza ku Yuda ndi kulalikira mu Yerusalemu kuti, ‘Lizani lipenga mʼdziko lonse!’ Ndipo fuwulani kuti, ‘Sonkhanani! Tiyeni tithawire ku mizinda yotetezedwa!’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Nenani m'Yuda, lalikirani m'Yerusalemu, ndi kuti, Ombani lipenga m'dzikomo; pfuulani, ndi kuti, Sonkhanani pamodzi, tilowe m'midzi ya malinga.