Jeremiah 4:8 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Motero valani ziguduli, mudandaule ndi kulira kwambiri. Pakuti mkwiyo woopsa wa Chauta sudatichoke.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Pamenepo, valani chiguduli, lirani ndi kubuula; pakuti mkwiyo wa kuopsa wa Yehova sunabwerera pa ife.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Choncho valani ziguduli, lirani ndi kubuwula, pakuti mkwiyo waukulu wa Yehova sunatichokere.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Pamenepo, bvalani ciguduli, lirani ndi kubuula; pakuti mkwiyo wakuopsya wa Yehova sunabwerera pa ife.