Jeremiah 40:12 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono Ayuda onsewo adabwera kuchokera ku maiko onse kumene adaabalalikira. Adabwerera ku Yuda nakadziwonetsa kwa Gedaliya ku Mizipa. Ndipo minda yao idabereka zipatso zambiri ndi vinyo wambiri.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
pamenepo Ayuda onse anabwerera kufumira ku malo onse kumene anawaingitsirako, nafika ku dziko la Yuda, kwa Gedaliya, ku Mizipa, nasonkhanitsa vinyo ndi zipatso zamalimwe zambiri.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono Ayuda onsewo anabwerera ku Yuda, ku Mizipa kwa Gedaliya, kuchokera ku mayiko onse kumene anabalalikira. Ndipo anakolola zipatso zochuluka ndi vinyo wambiri.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
pamenepo Ayuda onse anabwerera kufumira ku malo onse kumene anawaingitsirako, nafika ku dziko la Yuda, kwa Gedaliya, ku Mizipa, nasonkhanitsa vinyo ndi zipatso zamalimwe zambiri.