Jeremiah 40:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsiku lina Yohanani mwana wa Kareya, pamodzi ndi atsogoleri ankhondo amene sadadzipereke aja, adapita kwa Gedaliya ku Mizipa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndiponso Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala m'minda, anadza kwa Gedaliya ku Mizipa,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yohanani mwana wa Kareya ndi atsogoleri a ankhondo onse amene sanadzipereke aja anabwera ku Mizipa kwa Gedaliya
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndiponso Yohanani mwana wa Kareya, ndi akazembe onse a nkhondo okhala m'minda, anadza kwa Gedaliya ku Mizipa,