Jeremiah 40:6 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pamenepo Yeremiya adapita kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa. Ndipo adakhala naye pakati pa anthu otsala m'dzikomo.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo Yeremiya ananka kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa, nakhala kumeneko kwa anthu otsala m'dziko.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Motero Yeremiya anapita kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa ndipo anakakhala naye kumeneko pakati pa anthu amene anatsala mʼdzikomo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo Yeremiya ananka kwa Gedaliya mwana wa Ahikamu ku Mizipa, nakhala kumeneko kwa anthu otsala m'dziko.