Jeremiah 41:15 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma Ismaele mwana wa Netaniya, pamodzi ndi anthu ake asanu ndi atatu, adathaŵa Yohanani, kuthaŵira kwa Aamoni.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma Ismaele mwana wake wa Netaniya anapulumuka Yohanani ndi anthu asanu ndi atatu, nanka kwa ana a Amoni.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Koma Ismaeli pamodzi ndi anthu ake asanu ndi atatu, anathawa Yohanani ndi kuthawira kwa Aamoni.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma Ismayeli mwana wace wa Netaniya anapulumuka Yohanani ndi anthu asanu ndi atatu, nanka kwa ana a Amoni.