Jeremiah 42:1 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Atsogoleri onse a ankhondo, pamodzi ndi Yohanani mwana wa Kareya, Azariya mwana wa Hesaya, kudzanso anthu onse ang'onoang'ono ndi akuluakulu omwe, adapita kwa mneneri Yeremiya. Adamuuza kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo akazembe onse a nkhondo, ndi Yohanani mwana wake wa Kareya, ndi Yezaniya mwana wake wa Hosaya, ndi anthu onse kuyambira wamng'ono, kufikira wamkulu, anayandikira,
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Atsogoleri onse a ankhondo pamodzi ndi Yohanani mwana wa Kareya ndi Azariya mwana wa Hosayia, ndiponso anthu onse, ana ndi akuluakulu omwe, anapita
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo akazembe onse a nkhondo, ndi Yohanani mwana wace wa Kareya, ndi Jezaniya mwana wace wa Hosiya, ndi anthu onse kuyambira wamng'ono, kufikira wamkuru, anayandikira,