Jeremiah 42:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Ndidzakuchitirani chifundo, kotero kuti iyenso adzakuchitirani chifundo ndi kukulolani kuti mukhale m'dziko lanu lino.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo ndidzakuchitirani inu chifundo, kuti iye akuchitireni inu chifundo, nakubwezereni inu kudziko lanu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Ndidzakuchitirani chifundo, ndipo mfumuyonso idzakuchitirani chifundo ndi kukulolani kuti mukhale mʼdziko mwanumwanu.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo ndidzakucitirani inu cifundo, li kuti iye akucitireni inu cifundo, nakubwezereni inu ku dziko lanu.