Jeremiah 42:13 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Koma mwina simumvera mau a Chauta, nkunena kuti,
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Koma mukati, Sitidzakhala m'dziko muno; osamvera mau a Yehova Mulungu wanu;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Koma mwina simudzamvera Yehova Mulungu wanu nʼkumanena kuti, ‘Ayi ife sitidzakhala mʼdziko muno,
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Koma mukati, Sitidzakhala m'dziko muno; osamvera mau a Yehova Mulungu wanu;