Jeremiah 42:14 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
‘Ai, tipita ndithu ku Ejipitoko, kopanda nkhondo, kosamva kulira kwa lipenga, kosasoŵa chakudya, ndipo tidzakhala kumeneko.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
ndi kuti, Iai; tidzanka ku Ejipito, kumene sitidzaona nkhondo, sitidzamva kulira kwa lipenga, sitidzamva njala yokhumba mkate; pamenepo tidzakhala;
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
ndipo ngati mukunena kuti, ‘Ayi, koma tidzapita ku Igupto kumene sitidzaonako nkhondo kapena kumva kulira kwa lipenga kapenanso kusowa chakudya.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
ndi kuti, Iai; tidzanka ku Aigupto, kumene sitidzaona nkhondo, sitidzamva kulira kwa lipenga, sitidzamva njala yokhumba mkate; pamenepo tidzakhala;