Jeremiah 42:22 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Tsono mudziŵe kuti mudzafadi ndi nkhondo, njala ndiponso mliri, ku malo amene mufuna kupita kuti mukakhaleko.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Tsopano mudziwetu kuti mudzafa ndi lupanga, ndi njala ndi chaola, komwe mufuna kukakhalako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Tsono dziwani ichi: mudzafadi ndi nkhondo, njala ndi mliri kumalo kumene mukufuna mukakhaleko.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Tsopano mudziwetu kuti mudzafa ndi lupanga, ndi njala ndi caola, komwe mufuna kukakhalako.