Jeremiah 46:1 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chauta adauza mneneri Yeremiya mau onena za anthu a mitundu ina.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri akunena za amitundu.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Yehova anamupatsa Yeremiya uthenga wonena za anthu a mitundu ina.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya mneneri akunena za amitundu.