Jeremiah 46:11 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Pita ku Giliyadi, ukatenge mankhwala, namwali iwe Ejipito. Wayesayesa mankhwala ambiri koma walephera, matenda akowo sadzachira.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Kwera ku Giliyadi, tenga vunguti, namwali iwe mwana wa Ejipito; wachulukitsa mankhwala chabe; palibe kuchira kwako.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Pita ku Giliyadi ukatenge mankhwala iwe namwali Igupto. Wayesayesa mankhwala ambiri koma osachira; palibe mankhwala okuchiritsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Kwera ku Gileadi, tenga bvunguti, namwali iwe mwana wa Aigupto; wacurukitsa mankhwala cabe; palibe kucira kwako.