Jeremiah 46:12 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Anthu a mitundu ina amva za manyazi ako, kulira kwako kwadzaza dziko lapansi. Ankhondo akunka nagwetsanagwetsana, onse pansi ndu kugwera limodzi.”
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Amitundu amva manyazi anu, dziko lapansi ladzala ndi kufuula kwanu; pakuti amphamvu akhumudwitsana, agwa onse awiri pamodzi.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Anthu a mitundu ina amva za manyazi ako; kulira kwako kwadzaza dziko lapansi. Ankhondo akunka nagwetsanagwetsana, onse awiri agwa pansi limodzi.”
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Amitundu amva manyazi anu, dziko lapansi ladzala ndi kupfuula kwanu; pakuti amphamvu akhumudwitsana, agwa onse awiri pamodzi.