Jeremiah 46:13 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Naŵa mau amene Chauta adalankhula ndi mneneri Yeremiya za kubwera kwa Nebukadinezara, mfumu ya ku Babiloni, kudzathira nkhondo dziko la Ejipito:
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mau amene Yehova ananena kwa Yeremiya mneneri, kuti Nebukadinezara mfumu ya ku Babiloni adzafika adzakantha dziko la Ejipito.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Uthenga umene Yehova anapatsa mneneri Yeremiya wonena za kubwera kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni kudzathira nkhondo Igupto ndi uwu:
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mau amene Yehova ananena kwa Yeremiya mneneri, kuti Nebukadirezara mfumu ya ku Babulo adzafika adzakantha dziko la Aigupto.