Jeremiah 46:15 — Compare Translations
4 translations compared side by side
Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Chifukwa chiyani mulungu wanu Apisi wathaŵa? Chifukwa chiyani nkhunzi yanu yoipembedza ija sidalimbike? Nchifukwa choti Chauta waigwetsa.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Akulimba ako akokoledwa bwanji? Sanaime, chifukwa Yehova anawathamangitsa.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Chifukwa chiyani mulungu wanu wamphamvu uja Apisi wathawa? Iye sakanatha kulimba chifukwa Yehova anamugwetsa.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Akulimba ako akokoledwa bwanji? sanaime, cifukwa Yehova anawathamangitsa,