Jeremiah 46:17 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Farao, mfumu ya ku Ejipito, mpatseni dzina lakuti ‘Waphokoso, wotaya mwai wake.’
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ndipo anafuula kumeneko, Farao mfumu ya Aejipito ndiye phokoso lokha; wapititsa nthawi yopangira.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Kumeneku iwo adzafuwula kuti, ‘Farao, mfumu ya ku Igupto mupatseni dzina lakuti, Waphokoso, Wotaya mwayi wake.’
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Ndipo anapfuula kumeneko, Farao mfumu ya Aigupto ndiye phokoso lokha; wapititsa nthawi yopangira,