Jeremiah 46:19 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
Konzani katundu wanu wopita naye ku ukapolo, inu anthu a ku Ejipito, pakuti Memfisi adzasanduka chipululu, ngati bwinja, mopanda anthu.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Mwana wamkazi iwe wokhala m'Ejipito, dzikonzere kunka kundende; pakuti Nofi adzakhala bwinja, nadzapsa, mulibenso wokhalamo.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
Konzani katundu wanu wopita naye ku ukapolo inu anthu a ku Igupto, pakuti Mefisi adzasanduka chipululu ndipo adzakhala bwinja mopanda wokhalamo.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Mwana wamkazi iwe wokhala m'Aigupto, dzikonzere kunka kundende; pakuti Nofi adzakhala bwinja, nadzapsya, mulibenso wokhalamo.