Jeremiah 46:20 — Compare Translations

4 translations compared side by side

Chewa (Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa)
“Ejipito ali ngati mwanawang'ombe wokongola. Koma chimphanga chochokera kumpoto chidzamtera.
Chewa 1922 (Buku Lopatulika)
Ejipito ndi ng'ombe yaikazi yosalala; chionongeko chituluka kumpoto chafika, chafika.
Chewa 2002 (Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero)
“Igupto ali ngati mwana wangʼombe wokongola, koma chimphanga chikubwera kuchokera kumpoto kudzalimbana naye.
Chewa Bible (BL) 1992 - Buku Lopatulika
Aigupto ndi ng'ombe ya msoti yosalala; cionongeko cituruka kumpoto cafika, cafika.